1199

SERMON TOPIC: MAZIKO OKHAZIKIKA- 3 - CHIPHUNZITSO CHA UBATIZO

Speaker: David Makiyi

Language: CHICHEWA

Date: 7 June 2013

Topic Groups: 1ST PRINCIPLES

Sermon synopsis: Nthawi zambiri timakhala ndi chidziwitso cha ma ubatizo atatu akulu amuBaibulo. Koma tiyenera kudziwa kuti Baibulo limanenanso za ubatizo wa chinayi sikuyenera kukhala osaudziwa. Mu chiphunzitso chathu cha ‘Ubatizo’, tifotokozera magawo anai aubatizo amene akupezeka mmawu a Mulungu:
- Download notes (62 KB, 3244 downloads)

- Download audio (9.48 MB, 3400 downloads)
- All sermons by David Makiyi

- All sermons on 1ST PRINCIPLES

- All sermons in CHICHEWA




IP:Country:City:Region: